Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 32:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Kenako Elihu mwana wa Barakeli mbadwa ya Buza anati:

      “Ine ndine wamng’ono

      Ndipo amuna inu ndinu achikulire.+

      N’chifukwa chake ndinabweza mawu anga ndipo ndinaopa

      Kukuuzani zimene ndikudziwa.

  • Miyambo 23:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Mvera bambo ako amene anakubereka,+ ndipo usanyoze mayi ako chifukwa chakuti akalamba.+

  • Maliro 5:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Akalonga athu awapachika dzanja limodzi lokha.+ Anthuwo sanalemekezenso ngakhale amuna okalamba.+

  • 1 Timoteyo 5:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Usadzudzule mwamuna wachikulire mokalipa,+ koma umudandaulire ngati bambo ako. Amuna achinyamata uwadandaulire ngati abale ako,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena