-
Ekisodo 12:14Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 “‘Tsiku limeneli lidzakhala chikumbutso kwa inu, ndipo muzichitira Yehova chikondwerero m’mibadwo yanu yonse. Limeneli ndi lamulo mpaka kalekale, kuti muzichita chikondwerero chimenechi.
-