Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 22:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Ng’ombe kapena nkhosa, musaiphe tsiku limodzi ndi mwana wake.+

  • Salimo 36:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Inu Mulungu, chilungamo chanu chili ngati mapiri anu.+

      Chiweruzo chanu ndi chozama kwambiri ngati madzi akuya.+

      Inu Yehova, mumapulumutsa munthu ndiponso nyama.+

  • Salimo 145:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Yehova amakomera mtima aliyense,+

      Ndipo ntchito zake zonse amazichitira chifundo.+

  • Miyambo 12:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Wolungama amasamalira moyo wa chiweto chake,+ koma chisamaliro cha anthu oipa n’chankhanza.+

  • Mateyu 10:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Kodi mpheta ziwiri si paja amazigulitsa kakhobidi kamodzi kochepa mphamvu?+ Komatu palibe ngakhale imodzi imene idzagwa pansi Atate wanu osadziwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena