Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 30:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndipo Yehova Mulungu wako adzakuchititsa kukhala ndi zinthu zosefukira pa ntchito iliyonse ya manja ako,+ chipatso cha mimba yako, chipatso cha ziweto zako+ ndi chipatso cha nthaka yako.+ Pamenepo udzatukuka+ chifukwa Yehova adzakondweranso nawe kuti akuchitire zabwino, monga mmene anakondwera ndi makolo ako.+

  • Salimo 65:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Inu mwatembenukira dziko lapansi kuti mulipatse zinthu zochuluka,+

      Mwalilemeretsa kwambiri.

      Mtsinje wochokera kwa Mulungu ndi wosefukira ndi madzi.+

      Munalinganiza zinthu, kuti mbewu zawo zibale.+

      Umu ndi mmene mumaperekera zinthu padziko lapansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena