Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 28:63
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 63 “Chotero, monga mmene Yehova anasangalalira kuti akuchitireni zabwino ndi kukuchulukitsani,+ momwemonso adzasangalala kuti akuwonongeni ndi kukufafanizani.+ Pamenepo mudzatheratu m’dziko limene mukupita kukalitenga kukhala lanu.+

  • 1 Mafumu 14:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yehova adzawonongadi Isiraeli, ndipo zidzakhala ngati mmene bango limagwedezekera m’madzi,+ ndiponso adzazuladi+ Aisiraeli, kuwachotsa padziko labwinoli+ limene anapatsa makolo awo. Ndiyeno adzawabalalitsira+ kutsidya lina la Mtsinje,*+ popeza iwo anapanga mizati yawo yopatulika,+ n’kukwiyitsa+ nayo Yehova.

  • 2 Mafumu 17:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Chotero Yehova anawakwiyira kwambiri+ Aisiraeli ndipo anawachotsa pamaso pake.+ Sanasiye aliyense kupatulapo fuko la Yuda lokha.+

  • Salimo 52:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mulungu adzakupasula kosatha.+

      Adzakugwetsa ndi kukukokera kunja kwa hema wako,+

      Ndipo adzakuzula ndithu m’dziko la anthu amoyo.+ [Seʹlah.]

  • Luka 21:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Anthu adzaphedwa ndi lupanga ndiponso kutengedwa ukapolo kupita nawo ku mitundu ina yonse.+ Anthu a mitundu ina adzapondaponda Yerusalemu, kufikira nthawi zoikidwiratu+ za anthu a mitundu inawo zitakwanira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena