Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 25:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndipo mundipangire malo opatulika, popeza ndiyenera kukhala pakati panu.+

  • Levitiko 26:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Motero ndidzayendadi pakati panu ndi kukusonyezani kuti ine ndine Mulungu wanu,+ ndipo inu mudzakhala anthu anga.+

  • Deuteronomo 5:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Pakuti ndani mwa anthu onse amene anamvetserapo mawu a Mulungu wamoyo,+ akulankhula kuchokera pakati pa moto monga mmene tachitira ife n’kukhalabe ndi moyo?

  • Salimo 46:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Mulungu ndiye pothawira pathu ndi mphamvu yathu,+

      Thandizo lopezeka mosavuta pa nthawi ya masautso.+

  • Salimo 145:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Yehova ali pafupi ndi onse oitanira pa iye.+

      Iye ali pafupi ndi onse amene amamuitana m’choonadi,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena