Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 13:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Iwo anabwera kwa Mose ndi Aroni, ndiponso kwa khamu lonse la ana a Isiraeli m’chipululu cha Parana, ku Kadesi.+ Anafotokozera onsewo za ulendo wawo n’kuwaonetsa zipatso za kudzikolo.

  • Deuteronomo 9:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Yehova atakutumani kuchokera ku Kadesi-barinea+ kuti, ‘Kwerani ndi kukatenga dziko limene ndidzakupatsani kuti likhale lanu,’ pamenepo munapandukiranso malamulo a Yehova Mulungu wanu,+ ndipo simunasonyeze chikhulupiriro+ mwa iye komanso simunamvere mawu ake.+

  • Yoswa 14:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndinali ndi zaka 40 pamene Mose mtumiki wa Yehova anandituma kukazonda dziko,+ kuchokera ku Kadesi-barinea. Nditabwerako ndinamuuza kuchokera pansi pa mtima wanga, zonse zimene ndinaona.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena