Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 21:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Womenya abambo ake ndi mayi ake aziphedwa ndithu.+

  • Levitiko 19:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 “‘Aliyense wa inu aziopa mayi ndi bambo ake,+ ndipo muzisunga masabata anga.+ Ine ndine Yehova Mulungu wanu.

  • Deuteronomo 27:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “‘Wotembereredwa ndi munthu wonyoza bambo ake kapena mayi ake.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

  • Miyambo 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Mwana wanga, tamvera malangizo a bambo ako,+ ndipo usasiye malamulo a mayi ako,+

  • Maliko 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mwachitsanzo, Mose ananena kuti, ‘Uzilemekeza bambo ako ndi mayi ako,’+ komanso anati, ‘Aliyense wonenera bambo ake kapena mayi ake zachipongwe afe ndithu.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena