Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 20:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pambuyo pake Yehova anauza Mose ndi Aroni kuti: “Chifukwa simunasonyeze chikhulupiriro mwa ine, polephera kundilemekeza+ pamaso pa ana a Isiraeli, simudzaulowetsa mpingowu m’dziko limene ndidzawapatse.”+

  • Numeri 27:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pambuyo poliona dzikolo, udzaikidwa m’manda kuti ukagone ndi makolo ako.+ Ndithudi, iweyo udzaikidwa m’manda mofanana ndi Aroni m’bale wako,+

  • Deuteronomo 3:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Pamenepo Yehova anapitiriza kundikwiyira chifukwa cha inu,+ ndipo sanandimvere. Motero Yehova anandiuza kuti, ‘Basi khala chete! Usatchulenso nkhani imeneyi kwa ine.

  • Salimo 106:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Kuwonjezera pamenepo, iwo anaputa mkwiyo pa madzi a ku Meriba,+

      Moti Mose sizinamuyendere bwino chifukwa cha anthu amenewa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena