Ekisodo 33:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Pamenepo Mulungu anati: “Ineyo ndidzayenda nawe+ ndipo ndidzakupatsa mpumulo.”+ Yoswa 1:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 “Mukumbukire mawu amene Mose mtumiki wa Yehova anakulamulani,+ akuti, ‘Yehova Mulungu wanu akukupatsani mpumulo, ndipo wakupatsani dziko ili. Yoswa 11:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Chotero Yoswa analanda dziko lonse monga mmene Yehova analonjezera Mose.+ Ndiyeno Yoswa anapereka dzikolo kwa Aisiraeli monga cholowa chawo, malinga ndi magawo awo potsata mafuko awo.+ Ndipo dziko lonse linakhala bata, lopanda nkhondo.+ Yoswa 22:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Tsopano Yehova Mulungu wanu wapatsa abale anu mpumulo monga momwe anawalonjezera.+ Chotero bwererani, mupite kumahema anu m’dziko lanu, limene Mose mtumiki wa Yehova anakupatsani kutsidya lina la Yorodano.+ Miyambo 16:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Yehova akasangalala ndi njira za munthu,+ amachititsa ngakhale adani a munthuyo kukhala naye pa mtendere.+
13 “Mukumbukire mawu amene Mose mtumiki wa Yehova anakulamulani,+ akuti, ‘Yehova Mulungu wanu akukupatsani mpumulo, ndipo wakupatsani dziko ili.
23 Chotero Yoswa analanda dziko lonse monga mmene Yehova analonjezera Mose.+ Ndiyeno Yoswa anapereka dzikolo kwa Aisiraeli monga cholowa chawo, malinga ndi magawo awo potsata mafuko awo.+ Ndipo dziko lonse linakhala bata, lopanda nkhondo.+
4 Tsopano Yehova Mulungu wanu wapatsa abale anu mpumulo monga momwe anawalonjezera.+ Chotero bwererani, mupite kumahema anu m’dziko lanu, limene Mose mtumiki wa Yehova anakupatsani kutsidya lina la Yorodano.+
7 Yehova akasangalala ndi njira za munthu,+ amachititsa ngakhale adani a munthuyo kukhala naye pa mtendere.+