Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 1:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Amenewa ndiwo osankhidwa a khamu la anthuwo, atsogoleri a mafuko+ a makolo awo. Aliyense wa iwo ndi mtsogoleri wa anthu masauzande mu Isiraeli.”+

  • Deuteronomo 1:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Sankhani amuna anzeru, aluso+ ndi ozindikira+ m’mafuko anu, kuti ndiwaike kukhala atsogoleri anu.’+

  • Yoswa 14:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Limeneli ndilo dziko limene ana a Isiraeli anatenga monga cholowa chawo m’dziko la Kanani.+ Wansembe Eleazara, Yoswa mwana wa Nuni, ndi atsogoleri a mafuko a makolo a ana a Isiraeli, ndiwo anagawa dzikolo kuti likhale cholowa chawo.+

  • Yoswa 22:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Atamva zimenezi, ana a Rubeni, ana a Gadi, ndi hafu ya fuko la Manase anayankha+ atsogoleri a masauzande a Aisiraeli, kuti:+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena