Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Mdaniyo anati, ‘Ndiwathamangira,+ ndi kuwapeza!+

      Ndigawa chuma chawo.+ Pamenepo moyo wanga ukhutira ndi zimene ndawachita!

      Ndisolola lupanga langa! Dzanja langa liwawononga!’+

  • Oweruza 20:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Ana a Benjamini atatuluka kuti akakumane ndi anthuwo, anakokedwera kutali ndi mzinda.+ Ndiyeno monga mmene zinachitikira maulendo oyamba aja, ana a Benjaminiwo anayamba kukantha ena mwa anthuwo, amuna a Isiraeli 30,+ pamisewu ikuluikulu yakunja kwa mzinda, ndi kuwavulaza koti sakanatha kuchira. Wina mwa misewu imeneyi unali wopita ku Beteli+ ndipo wina unali wopita ku Gibeya.+

  • Salimo 9:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yehova amadziwika ndi ziweruzo zimene amapereka.+

      Woipa wakodwa mumsampha wa ntchito ya manja ake.+

      Higayoni.* [Seʹlah.]

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena