Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 13:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Tinaonakonso Anefili,* mbadwa za Anaki,+ moti eni akefe tinangodziona ngati tiziwala kwa iwo. Iwonso ndi mmene anationera.”+

  • Yoswa 11:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Kuwonjezera apo, pa nthawiyo Yoswa anapita n’kukafafaniziratu Aanaki.+ Aanakiwo anali kukhala kudera lamapiri, ku Heburoni, ku Debiri, ku Anabi,+ kudera lonse lamapiri la Yuda ndiponso kudera lonse lamapiri la Isiraeli.+ Yoswa anafafaniziratu Aanakiwo pamodzi ndi mizinda yawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena