Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 26:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Ana aamuna a Manase+ anali Makiri+ amene anali kholo la banja la Amakiri. Makiri anabereka Giliyadi.+ Giliyadi anali kholo la banja la Agiliyadi.

  • 1 Mbiri 2:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Kenako Gesuri+ ndi Siriya+ analanda Havoti-yairi.+ Analandanso Kenati+ ndi midzi yake yozungulira, mizinda 60. Onsewa anali ana a Makiri, bambo wa Giliyadi.

  • 1 Mbiri 7:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mwana wa Manase+ yemwe mdzakazi wake wachisiriya anam’berekera, anali Asiriyeli. (Mdzakaziyo anabereka Makiri,+ bambo wa Giliyadi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena