1 Samueli 28:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ndiyeno Afilisiti anasonkhana pamodzi ndi kupita kukamanga msasa ku Sunemu.+ Nayenso Sauli anasonkhanitsa Aisiraeli onse pamodzi ndi kumanga msasa ku Giliboa.+ 1 Mafumu 1:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ndiyeno anakafunafuna mtsikana wokongola m’dziko lonse la Isiraeli. Pamapeto pake anapeza Abisagi+ Msunemu+ n’kubwera naye kwa mfumu. 1 Mafumu 2:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Adoniya anapitiriza kuti: “Chonde, mukauze Mfumu Solomo kuti andipatse Abisagi+ Msunemu+ akhale mkazi wanga. Ndikudziwa kuti inuyo sakakukanirani.” 2 Mafumu 4:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Tsiku lina Elisa anapita ku Sunemu.+ Kumeneko kunali mayi wina wodziwika. Mayiyo anaumiriza+ Elisa kuti adye chakudya. Nthawi zonse Elisa akamadutsa, anali kupatukira kumeneko kukadya chakudya.
4 Ndiyeno Afilisiti anasonkhana pamodzi ndi kupita kukamanga msasa ku Sunemu.+ Nayenso Sauli anasonkhanitsa Aisiraeli onse pamodzi ndi kumanga msasa ku Giliboa.+
3 Ndiyeno anakafunafuna mtsikana wokongola m’dziko lonse la Isiraeli. Pamapeto pake anapeza Abisagi+ Msunemu+ n’kubwera naye kwa mfumu.
17 Adoniya anapitiriza kuti: “Chonde, mukauze Mfumu Solomo kuti andipatse Abisagi+ Msunemu+ akhale mkazi wanga. Ndikudziwa kuti inuyo sakakukanirani.”
8 Tsiku lina Elisa anapita ku Sunemu.+ Kumeneko kunali mayi wina wodziwika. Mayiyo anaumiriza+ Elisa kuti adye chakudya. Nthawi zonse Elisa akamadutsa, anali kupatukira kumeneko kukadya chakudya.