Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 19:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Malire a gawo lawo anakafika ku Yezereeli,+ Kesulotu, Sunemu,+

  • 1 Mafumu 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno anakafunafuna mtsikana wokongola m’dziko lonse la Isiraeli. Pamapeto pake anapeza Abisagi+ Msunemu+ n’kubwera naye kwa mfumu.

  • 2 Mafumu 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Tsiku lina Elisa anapita ku Sunemu.+ Kumeneko kunali mayi wina wodziwika. Mayiyo anaumiriza+ Elisa kuti adye chakudya. Nthawi zonse Elisa akamadutsa, anali kupatukira kumeneko kukadya chakudya.

  • Nyimbo ya Solomo 6:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “Bwerera, bwerera iwe Msulami! Bwerera, bwerera kuti tikuone!”+

      “Kodi anthu inu mukuona chiyani mwa ine Msulami?”+

      “Tikuona ngati tikuonerera gule wa magulu awiri a anthu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena