-
2 Samueli 11:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 Ndani uja anapha Abimeleki+ mwana wa Yerubeseti?*+ Kodi si mkazi amene anaponya mwala wokhala pamwamba wa mphero+ ali pamwamba pa mpanda, ndipo Abimeleki anafera ku Tebezi+ komweko? N’chifukwa chiyani amuna inu munauyandikira kwambiri mpandawo?’ Pamenepo ukanene kuti, ‘Nayenso Uriya Mhiti, mtumiki wanu, wafa.’”+
-