Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 15:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno Abisalomu anali kupitiriza kunena kuti: “Haa! Zikanakhalatu bwino ndikanaikidwa kukhala woweruza m’dziko lino+ kuti munthu aliyense wokhala ndi mlandu kapena wofuna chiweruzo azibwera kwa ine, ndipo ndikanamuchitira chilungamo.”+

  • Salimo 10:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pakuti woipa amadzitamandira ndi zilakolako zake zadyera,+

      Ndipo wopanga phindu lachinyengo+ amadzitamanda.

      נ [Nun]

      Iye amanyoza Yehova.+

  • Aroma 1:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 ndi miseche.+ Anakhala odana ndi Mulungu, achipongwe,+ odzikweza,+ odzimva,+ oyambitsa zoipa,+ osamvera makolo,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena