Genesis 18:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Popeza mwadzera njira yodutsa kwa kapolo wanu, mundilole ndikukonzereni kachakudya kuti mutsitsimutse mitima yanu.+ Mukatero mukhoza kupitiriza ulendo wanu.” Pamenepo iwo anati: “Chabwino, chita mmene waneneramo.” Genesis 18:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Kenako, Abulahamu anathamangira kumene kunali ziweto, n’kutengako ng’ombe yaing’ono yamphongo yonona. Atatero, anaipereka kwa wantchito wake, ndipo iye anaikonza mwamsanga.+ Oweruza 6:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Chonde musachoke, kufikira nditabwera+ ndi kukupatsani mphatso yanga.”+ Choncho iye anati: “Ineyo ndikhalabe pompano kufikira utabweranso.” Aheberi 13:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Musaiwale kuchereza alendo,+ pakuti potero, ena anachereza angelo mosadziwa.+
5 Popeza mwadzera njira yodutsa kwa kapolo wanu, mundilole ndikukonzereni kachakudya kuti mutsitsimutse mitima yanu.+ Mukatero mukhoza kupitiriza ulendo wanu.” Pamenepo iwo anati: “Chabwino, chita mmene waneneramo.”
7 Kenako, Abulahamu anathamangira kumene kunali ziweto, n’kutengako ng’ombe yaing’ono yamphongo yonona. Atatero, anaipereka kwa wantchito wake, ndipo iye anaikonza mwamsanga.+
18 Chonde musachoke, kufikira nditabwera+ ndi kukupatsani mphatso yanga.”+ Choncho iye anati: “Ineyo ndikhalabe pompano kufikira utabweranso.”