Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 16:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pamenepa n’kuti anthu atabisalira Samisoni m’chipinda cha mkaziyo,+ ndipo mkaziyo anamuuza kuti: “Afilisiti+ aja abwera Samisoni!” Pamenepo Samisoni anadula zingwe zija pakati, monga mmene ulusi wopota wabwazi umadukira ukayandikira moto.+ Ndipo chinsinsi cha mphamvu zake sichinadziwike.+

  • Oweruza 16:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndiyeno Delila anatenga zingwe zatsopano ndi kum’manga nazo, n’kumuuza kuti: “Afilisiti aja abwera Samisoni!” Pa nthawiyi n’kuti anthu atam’bisalira m’chipinda cha mkaziyo.+ Pamenepo, Samisoni anadula pakati zingwe zimene anam’manga nazo manjazo, ngati kuti akudula ulusi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena