Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 19:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Sauli anamvera mawu a Yonatani, ndipo analumbira kuti: “Pali Yehova, Mulungu wamoyo,+ Davide saphedwa.”

  • Salimo 79:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mverani kuusa moyo kwa mkaidi.+

      Anthu opita kukaphedwa muwateteze ndi dzanja lanu lamphamvu.+

  • Mlaliki 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mwana wosauka koma wanzeru ali bwino+ kuposa mfumu yokalamba koma yopusa,+ imene sionanso kufunika kochenjezedwa.+

  • Mlaliki 8:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 chifukwa mawu a mfumu ali ndi mphamvu yolamulira,+ ndipo ndani angaifunse kuti: ‘Kodi mukuchita chiyani?’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena