Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 22:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Amuna onse amene anali kusautsidwa,+ onse amene anali ndi ngongole,+ ndi onse amene anali ndi zodandaula+ anayamba kusonkhana kwa iye,+ ndipo iye anakhala mtsogoleri wawo.+ Anthu onse amene anali naye anakwana 400.

  • Yesaya 32:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 pakuti munthu wopusa adzalankhula zinthu zopanda nzeru,+ ndipo mtima wake udzaganiza zochita zinthu zopweteka ena.+ Iye adzachita zimenezi kuti azichita zopanduka,+ kuti azinenera Yehova zoipa, kuti achititse mimba ya munthu wanjala kukhala yopanda kanthu,+ ndiponso kuti achititse munthu waludzu kukhala wopanda chilichonse choti amwe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena