Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 20:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndiyeno ndidzatumiza mtumiki kuti, ‘Pita ukatole miviyo.’ Koma mtumikiyo ndikadzamuuza mawu akuti, ‘Mivi ili kumbali yakutiyakuti, pita ukatole,’ iweyo ukatuluke chifukwa ndiye kuti zinthu zili bwino ndipo palibe chodetsa nkhawa chilichonse. Ndikulumbira pali Yehova, Mulungu wamoyo.+

  • 1 Mafumu 2:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Tsopano m’dzina la Yehova Mulungu wamoyo,+ amene wandichititsa kukhazikika,+ amene wandiika pampando wachifumu wa Davide bambo anga,+ ndiponso amene anandipatsa mzere wa banja lachifumu+ monga ananenera,+ lero Adoniya aphedwa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena