-
Esitere 1:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Masiku amenewa atatha, mfumu inakonza phwando la masiku 7 m’munda wamaluwa, pabwalo la nyumba yake. Phwandoli inakonzera anthu onse okhala kunyumba ya mfumu yokhala ndi mpanda wolimba kwambiri ya ku Susani, anthu olemekezeka ndi anthu wamba omwe.
-