Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 13:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Patapita zaka ziwiri zathunthu, anthu ena anali kumeta ubweya wa nkhosa+ za Abisalomu ku Baala-hazori, pafupi ndi Efuraimu.+ Choncho Abisalomu anaitanira ana onse aamuna a mfumu kumeneko.+

  • 1 Mafumu 4:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Chakudya cha kunyumba yachifumu ya Solomo tsiku lililonse chinkakhala ufa wosalala wokwana miyezo 30 ya kori,*+ ufa wamba wokwana miyezo 60 ya kori,

  • Esitere 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Masiku amenewa atatha, mfumu inakonza phwando la masiku 7 m’munda wamaluwa, pabwalo la nyumba yake. Phwandoli inakonzera anthu onse okhala kunyumba ya mfumu yokhala ndi mpanda wolimba kwambiri ya ku Susani, anthu olemekezeka ndi anthu wamba omwe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena