-
1 Mafumu 1:25Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
25 Chifukwatu lero wapita kukapereka nsembe+ zambiri, za ng’ombe zamphongo, ana a ng’ombe onenepa, ndi nkhosa. Waitananso ana onse a mfumu, akulu a asilikali ndi wansembe Abiyatara.+ Moti panopa ali kumeneko ndipo akudya ndi kumwa pamaso pake n’kumanena kuti, ‘Mfumu Adoniya ikhale ndi moyo wautali!’+
-