Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Kubwezera ndi kwanga, chilangonso ndi changa.+

      Pa nthawi yoikidwiratu phazi lawo lidzaterereka poyenda,+

      Pakuti tsiku la tsoka lawo layandikira,+

      Ndipo zowagwera zikufika mofulumira.’+

  • 1 Samueli 24:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Yehova akhale woweruza, ndipo aweruze pakati pa ine ndi inu. Iye adzandiweruzira mlanduwu+ ndi kuchitapo kanthu kuti andimasule m’manja mwanu.”

  • Salimo 35:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Weruzani mlandu wanga inu Yehova, motsutsana ndi adani anga.+

      Menyani nkhondo ndi kugonjetsa amene akumenyana ndi ine.+

  • Salimo 43:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Ndiweruzeni+ inu Mulungu,

      Weruzani mlandu wanga+ motsutsana ndi mtundu wosakhulupirika.

      Ndipulumutseni kwa munthu wachinyengo ndi wochita zosalungama.+

  • Miyambo 22:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pakuti Yehova adzawateteza pa mlandu wawo,+ ndipo adzalanda moyo wa amene akuwabera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena