Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 9:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Kenako Farao anatumiza atumiki ake kukaitana Mose ndi Aroni ndi kuwauza kuti: “Tsopano ndachimwa.+ Yehova ndi wolungama,+ koma ine ndi anthu anga ndife olakwa.

  • 1 Samueli 15:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Pamenepo Sauli anayankha Samueli kuti: “Ndachimwa,+ ndaphwanya lamulo la Yehova komanso sindinamvere mawu anu, chifukwa ndinaopa anthu+ ndipo ndamvera mawu awo.

  • 1 Samueli 24:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Iye anapitiriza kuuza Davide kuti: “Ndiwe wolungama kwambiri kuposa ine,+ pakuti iwe wandichitira zabwino,+ koma ine ndakuchitira zoipa.

  • Mateyu 27:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Iye anati: “Ndachimwa popereka munthu wolungama.”*+ Koma iwo anamuyankha kuti: “Ife sizikutikhudza zimenezo. Udziwa wekha chochita!”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena