Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 2:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndipo iye anali kuwauza kuti:+ “Mukuchitiranji zinthu zoterezi?+ Chifukwatu anthu onse akundiuza zinthu zoipa zokhazokha zokhudza inu.+

  • Miyambo 19:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Langa mwana wako padakali chiyembekezo,+ ndipo usalakelake imfa yake.+

  • Mlaliki 8:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Popeza anthu ochita zoipa sanalangidwe msanga,+ n’chifukwa chake mtima wa ana a anthu wakhazikika pa kuchita zoipa.+

  • 1 Timoteyo 5:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Anthu amene ali ndi chizolowezi chochita tchimo,+ uwadzudzule+ pamaso pa onse kuti ena onse akhale ndi mantha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena