Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Mulungu anapitiriza kuti: “Ngati sakakukhulupirira ndi kulabadira chizindikiro choyamba, akakhulupirira chizindikiro chachiwirichi.+

  • 1 Samueli 10:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndiyeno zimene zinachitika n’zakuti, Sauli atangotembenuka kuti asiyane ndi Samueli, Mulungu anayamba kusintha mtima wake kukhala wina,+ moti zizindikiro+ zonsezi zinayamba kuchitikadi pa tsiku limenelo.

  • Yeremiya 44:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 “Yehova wanena kuti: ‘Tsopano chizindikiro cha zimenezi kwa inu ndi ichi,+ ine ndikulangani m’dziko lino kuti mudziwe kuti mawu anga adzakwaniritsidwadi moti ndidzakugwetserani tsoka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena