Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 23:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Katatu pa chaka muzindichitira chikondwerero.+

  • Ekisodo 34:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 “Katatu pa chaka, mwamuna aliyense pakati panu azionekera+ kwa Ambuye woona, Yehova, Mulungu wa Isiraeli.

  • Deuteronomo 12:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 koma mudzafunefune malo amene Yehova Mulungu wanu adzasankhe pakati pa mafuko anu onse kuti aikepo dzina lake, kuti lizikhala pamenepo. Amenewo ndiwo malo amene muzidzapitako.+

  • Yoswa 18:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kenako khamu lonse la ana a Isiraeli linasonkhana ku Silo,+ ndipo kumeneko anamangako chihema chokumanako,+ popeza anali atagonjetsa dziko lomwe linali pamaso pawo.+

  • Oweruza 21:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pamapeto pake anati: “Pajatu ku Silo+ kumachitika chikondwerero cha Yehova chaka ndi chaka. Mzinda wa Silo uli kum’mwera kwa Beteli, chakum’mawa kwa msewu waukulu wochokera ku Beteli kupita ku Sekemu,+ ndiponso chakum’mwera kwa Lebona.”

  • Luka 2:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Tsopano chaka ndi chaka makolo ake anali kukonda kupita ku Yerusalemu,+ ku chikondwerero cha pasika.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena