Genesis 47:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Kenako Yosefe anabweretsa bambo ake Yakobo n’kuwasonyeza kwa Farao. Ndipo Yakobo anadalitsa Farao.+ Rute 2:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Kenako Boazi anafika kuchokera ku Betelehemu ndipo anauza okololawo kuti: “Yehova akhale nanu.”+ Iwo anayankha mwa nthawi zonse kuti: “Yehova akudalitseni.”+ 1 Samueli 15:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Patapita nthawi Samueli anam’peza Sauli, ndipo Sauli anauza Samueli kuti: “Yehova akudalitseni.+ Ndachita zimene Yehova ananena.”+ 1 Samueli 25:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Izi zili choncho, mmodzi mwa anyamata a Nabala anauza Abigayeli, mkazi wa Nabala kuti: “Davide anatumiza nthumwi zake kuchokera m’chipululu kudzafunira zabwino mbuyanga, koma mbuyanga walalatira+ nthumwizo.
7 Kenako Yosefe anabweretsa bambo ake Yakobo n’kuwasonyeza kwa Farao. Ndipo Yakobo anadalitsa Farao.+
4 Kenako Boazi anafika kuchokera ku Betelehemu ndipo anauza okololawo kuti: “Yehova akhale nanu.”+ Iwo anayankha mwa nthawi zonse kuti: “Yehova akudalitseni.”+
13 Patapita nthawi Samueli anam’peza Sauli, ndipo Sauli anauza Samueli kuti: “Yehova akudalitseni.+ Ndachita zimene Yehova ananena.”+
14 Izi zili choncho, mmodzi mwa anyamata a Nabala anauza Abigayeli, mkazi wa Nabala kuti: “Davide anatumiza nthumwi zake kuchokera m’chipululu kudzafunira zabwino mbuyanga, koma mbuyanga walalatira+ nthumwizo.