Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 18:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Zitatero, Sauli anachita mantha+ ndi Davide chifukwa Yehova anali ndi Davideyo,+ koma Sauliyo anali atam’chokera.+

  • 1 Samueli 28:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pamenepo “Samueli” anafunsa Sauli kuti: “N’chifukwa chiyani wandisokoneza ndi kundidzutsa?”+ Sauli anayankha kuti: “Zinthu zandivuta kwambiri,+ pakuti Afilisiti akumenyana nane ndipo Mulungu wandichokera+ moti sakundiyankhanso, kaya kudzera mwa aneneri kapena m’maloto.+ N’chifukwa chake ndabwera kudzafunsa inu kuti mundiuze zimene ndiyenera kuchita.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena