1 Samueli 17:37 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 37 Ndiyeno Davide anawonjezera kuti: “Yehova amene anandilanditsa m’kamwa mwa mkango ndi m’kamwa mwa chimbalangondo andilanditsanso m’manja mwa Mfilisiti ameneyu.”+ Pamenepo Sauli anauza Davide kuti: “Pita, ndipo Yehova akhale nawe.”+ 2 Samueli 21:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Anthu anayi amenewa anali mbadwa za Arefai ku Gati.+ Iwo anaphedwa ndi dzanja la Davide ndi la atumiki ake.+ 2 Samueli 22:39 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 39 Ndidzawawononga onse ndi kuwaphwanya zibenthuzibenthu+ kuti asadzukenso.+Iwo adzagwa pansi ndipo ndidzawapondaponda ndi mapazi anga.+ Salimo 44:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Ndinu amene munatipulumutsa kwa adani athu,+Ndipo munanyazitsa anthu amene amadana nafe kwambiri.+
37 Ndiyeno Davide anawonjezera kuti: “Yehova amene anandilanditsa m’kamwa mwa mkango ndi m’kamwa mwa chimbalangondo andilanditsanso m’manja mwa Mfilisiti ameneyu.”+ Pamenepo Sauli anauza Davide kuti: “Pita, ndipo Yehova akhale nawe.”+
22 Anthu anayi amenewa anali mbadwa za Arefai ku Gati.+ Iwo anaphedwa ndi dzanja la Davide ndi la atumiki ake.+
39 Ndidzawawononga onse ndi kuwaphwanya zibenthuzibenthu+ kuti asadzukenso.+Iwo adzagwa pansi ndipo ndidzawapondaponda ndi mapazi anga.+