Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 7:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Usachite nawo mantha pakuti Yehova Mulungu wako, Mulungu wamphamvu ndi wochititsa mantha,+ ali pakati panu.+

  • 2 Mafumu 6:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma iye anati: “Usaope,+ popeza ife tili ndi ambiri kuposa amene ali ndi iwowo.”+

  • Salimo 18:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Ndidzaitanira pa Yehova, Iye woyenera kutamandidwa,+

      Ndipo adzandipulumutsa kwa adani anga.+

  • Salimo 115:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Inu oopa Yehova, khulupirirani Yehova.+

      Iye ndiye thandizo lanu ndi chishango chanu.+

  • 2 Akorinto 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iye anatipulumutsadi ku chinthu choopsa, ndicho imfa, ndipo adzatipulumutsabe.+ Tikukhulupirira kuti iye apitiriza kutipulumutsa.+

  • Aheberi 11:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Anagonjetsa mphamvu ya moto,+ anathawa lupanga,+ anali ofooka koma anapatsidwa mphamvu,+ analimba mtima pa nkhondo,+ ndiponso anagonjetsa magulu ankhondo a mayiko ena.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena