Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 60:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndi thandizo la Mulungu, tidzalandira mphamvu,+

      Ndipo Mulungu adzapondereza adani athu.+

  • Salimo 108:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndi thandizo la Mulungu, tidzalandira mphamvu,+

      Ndipo Mulungu adzapondereza adani athu.+

  • Ezekieli 32:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Kodi amenewa sadzagona limodzi ndi anthu amphamvu+ amene anaphedwa pakati pa anthu osadulidwa? Kodi sadzagona limodzi ndi anthu amene anatsikira ku Manda limodzi ndi zida zawo zankhondo? Mitu yawo idzatsamira malupanga awo ndipo mafupa awo adzalangidwa chifukwa cha zolakwa zawo,+ chifukwa anthu amphamvuwo anachititsa mantha anthu m’dziko la anthu amoyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena