Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 27:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndaleka kumukwiyira.+ Munthu wina akaika zitsamba zaminga ndi udzu pamaso panga,+ ndidzazipondaponda ndi kuzitentha nthawi imodzi ndipo ndidzamenyana naye.+

  • Mateyu 13:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Chotero, monga momwe amasonkhanitsira namsongole ndi kumutentha pamoto, zidzakhalanso choncho pa mapeto a nthawi* ino.+

  • Yohane 15:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ngati munthu sakhala wolumikizika kwa ine, amaponyedwa kunja monga nthambi ndipo amauma. Nthambi zoterozo anthu amazisonkhanitsa ndi kuziponya pamoto ndipo zimapsa.+

  • Aheberi 6:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Koma ikatulutsa minga ndi mitula, imakanidwa ndipo imatsala pang’ono kutembereredwa.+ Mapeto ake imatenthedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena