Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 15:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Koma Davide+ ndi akulu a Isiraeli+ ndiponso atsogoleri+a anthu 1,000 aliyense, anali kuyenda mosangalala+ kupita kunyumba kwa Obedi-edomu,+ kukatenga likasa la pangano la Yehova.

  • Salimo 24:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 “Tukulani mitu yanu, inu zipata,+

      Ndipo dzitukuleni, inu makomo akale lomwe,+

      Kuti Mfumu yaulemerero ilowe!”+

  • Salimo 68:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Iwo aona magulu anu a anthu opambana akuyendera pamodzi, inu Mulungu,+

      Magulu a anthu oyendera pamodzi a Mulungu wanga, Mfumu yanga, akukalowa kumalo oyera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena