Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 17:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Dzina lanu+ likhale lokhulupirika ndi lokwezeka+ mpaka kalekale. Anthu anene kuti, ‘Yehova wa makamu+ Mulungu wa Isiraeli,+ ndiye Mulungu wa Isiraeli,’+ ndipo nyumba ya mtumiki wanu Davide ikhalitse pamaso panu.+

  • 1 Mbiri 29:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Inu Yehova, ukulu,+ mphamvu,+ kukongola,+ ulemerero,+ ndi ulemu+ ndi zanu, chifukwa zinthu zonse zakumwamba ndi za padziko lapansi ndi zanu.+ Ufumu+ ndi wanu, inu Yehova, ndinunso Wokwezeka monga mutu pa onse.+

  • Salimo 72:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Lidalitsike dzina lake laulemerero mpaka kalekale,+

      Ndipo ulemerero wake udzaze dziko lonse lapansi.+

      Ame! Ame!*

  • Mateyu 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Koma inu muzipemphera motere:+

      “‘Atate wathu wakumwamba, dzina+ lanu liyeretsedwe.+

  • Yohane 12:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Atate lemekezani dzina lanu.” Pamenepo mawu+ anamveka kuchokera kumwamba kuti: “Ndalilemekeza ndipo ndidzalilemekezanso.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena