Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 11:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Davide atapha+ anthu a ku Zoba, Rezoni anayamba kusonkhanitsa anthu kumbali yake, ndipo anakhala mtsogoleri wa gulu la achifwamba. Chotero iye ndi gulu lakelo anapita kukakhala ku Damasiko,+ n’kuyamba kulamulira kumeneko.

  • Yesaya 7:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pakuti mutu wa Siriya ndiwo Damasiko, ndipo mutu wa Damasiko ndiwo Rezini. Pakamatha zaka 65, Efuraimu adzakhala ataphwanyidwaphwanyidwa moti sadzakhalanso mtundu wa anthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena