Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 14:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Usiku iye anagawa m’magulu asilikali akewo,+ omwe anali akapolo ake, kuti amenyane ndi adaniwo. Ndipo anawagonjetsa, moti anawapitikitsa mpaka ku Hoba, kumpoto kwa Damasiko.

  • 1 Mafumu 19:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako Yehova anamuuza kuti: “Nyamuka, bwerera udzere kuchipululu cha Damasiko.+ Pita ukadzoze+ Hazaeli+ kuti akhale mfumu ya Siriya.

  • 1 Mafumu 20:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Tsopano Beni-hadadi anauza Ahabu kuti: “Ndibweza mizinda+ imene bambo anga analanda bambo anu, ndipo inuyo mutenga misewu ku Damasiko mofanana ndi mmene bambo anga anatengera misewu ku Samariya.”

      Ahabu anayankha kuti: “Tikapanga pangano+ loti udzachitadi zimenezi, ndikusiya kuti uzipita kwanu.”

      Atatero anachita naye pangano ndipo anamuuza kuti azipita kwawo.

  • Yesaya 7:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pakuti mutu wa Siriya ndiwo Damasiko, ndipo mutu wa Damasiko ndiwo Rezini. Pakamatha zaka 65, Efuraimu adzakhala ataphwanyidwaphwanyidwa moti sadzakhalanso mtundu wa anthu.+

  • Machitidwe 9:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 kukamupempha zikalata za chilolezo zopita nazo kumasunagoge a ku Damasiko. Anapempha zikalatazo kuti akakapeza wina aliyense wotsatira Njirayo,*+ mwamuna kapena mkazi, akabwere naye ku Yerusalemu ali womangidwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena