Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 3:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mwa Arefai+ onse, Ogi yekha mfumu ya Basana ndi amene anali atatsala. Chithatha chimene anaikapo mtembo wake chinali chachitsulo. Kodi si chija chili ku Raba+ wa ana a Aamoni? N’chachitali mikono* 9, ndipo m’lifupi mwake mikono inayi, kutsatira muyezo wodziwika.

  • Deuteronomo 23:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Musachite kanthu kowathandiza kupeza mtendere ndi chitukuko masiku onse a moyo wanu, mpaka kalekale.+

  • Yoswa 13:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Gawo lawo linayambira kumzinda wa Yazeri,+ mizinda yonse ya ku Giliyadi,+ ndi hafu ya dziko la ana a Amoni,+ mpaka kukafika ku Aroweli+ kufupi ndi Raba.+

  • Yeremiya 49:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 “‘Fuula+ iwe Hesiboni+ pakuti mzinda wa Ai wafunkhidwa zinthu zake! Lirani inu midzi yozungulira Raba. Valani ziguduli.+ Lirani mokuwa ndi kuyendayenda m’makola amiyala chifukwa Malikamu adzatengedwa kupita ku ukapolo+ pamodzi ndi ansembe ndi akalonga ake onse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena