Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 12:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Sihoni+ mfumu ya Aamori, yemwe ankakhala ku Hesiboni.+ Dera lomwe anali kulamulira linkayambira pakatikati pa chigwa cha Arinoni kuphatikizapo mzinda wa Aroweli,+ umene unali m’mphepete mwa mtsinje wa Arinoni,+ mpaka hafu ya Giliyadi kukalekezera kuchigwa cha Yaboki,+ kumalire ndi ana a Amoni.

  • Oweruza 11:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndiyeno mfumu ya ana a Amoni inauza amithenga a Yefita kuti: “N’chifukwa chakuti Aisiraeli analanda dziko langa atatuluka mu Iguputo.+ Analanda dzikoli kuyambira ku Arinoni+ mpaka ku Yaboki ndi kukafikanso ku Yorodano.+ Tsopano undibwezere dzikoli mwamtendere.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena