-
1 Mafumu 8:25Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
25 Tsopano inu Yehova Mulungu wa Isiraeli, sungani lonjezo limene munalonjeza mtumiki wanu Davide bambo anga lakuti, ‘Anthu a m’banja lako sadzasiya kukhala pamaso panga, pampando wachifumu wa Isiraeli.+ Chofunika n’choti ana ako asamale mayendedwe awo mwa kuyenda pamaso panga monga momwe iwe wayendera pamaso panga.’
-