Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 1:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Komanso, Solomo wakhala pampando wachifumu.+

  • 1 Mbiri 29:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Chotero, Solomo anayamba kukhala pampando wachifumu wa Yehova+ monga mfumu m’malo mwa Davide bambo wake, ndipo ankalamulira bwino.+ Aisiraeli onse anali kumumvera.

  • 2 Mbiri 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Solomo mwana wa Davide anapitiriza kukhala wamphamvu mu ufumu wake.+ Yehova Mulungu wake anali naye,+ ndipo anapitiriza kumukulitsa kuposa wina aliyense.+

  • Salimo 132:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ana ako akadzasunga pangano langa+

      Ndi zikumbutso zanga zimene ndidzawapatsa,+

      Ngakhalenso ana awo+

      Adzakhala pampando wako wachifumu kwamuyaya.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena