1 Samueli 23:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ndiyeno zimene zinachitika n’zakuti, pamene Abiyatara+ mwana wamwamuna wa Ahimeleki anathawira kwa Davide ku Keila, anapita kumeneko atatenga efodi+ m’manja mwake. 2 Samueli 15:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Kumeneko kunalinso Zadoki+ pamodzi ndi Alevi+ onse atanyamula+ likasa+ la pangano la Mulungu woona. Choncho Aleviwo anatula pansi likasa la Mulungu woona pafupi ndi Abiyatara+ kufikira anthu onse atamaliza kudutsa kuchokera mumzinda. 1 Mbiri 15:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Tsopano Davide anawauza kuti: “Inuyo ndinu atsogoleri+ a nyumba ya makolo a Alevi. Choncho inu ndi abale anu mudziyeretse,+ ndipo mukatenge likasa la Yehova Mulungu wa Isiraeli n’kukaliika kumalo amene ine ndakonza kuti likakhaleko.
6 Ndiyeno zimene zinachitika n’zakuti, pamene Abiyatara+ mwana wamwamuna wa Ahimeleki anathawira kwa Davide ku Keila, anapita kumeneko atatenga efodi+ m’manja mwake.
24 Kumeneko kunalinso Zadoki+ pamodzi ndi Alevi+ onse atanyamula+ likasa+ la pangano la Mulungu woona. Choncho Aleviwo anatula pansi likasa la Mulungu woona pafupi ndi Abiyatara+ kufikira anthu onse atamaliza kudutsa kuchokera mumzinda.
12 Tsopano Davide anawauza kuti: “Inuyo ndinu atsogoleri+ a nyumba ya makolo a Alevi. Choncho inu ndi abale anu mudziyeretse,+ ndipo mukatenge likasa la Yehova Mulungu wa Isiraeli n’kukaliika kumalo amene ine ndakonza kuti likakhaleko.