Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 17:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma asadzichulukitsire mahatchi+ kapena kuchititsa anthu kubwerera ku Iguputo kuti akakhale ndi mahatchi ochuluka+ pakuti Yehova wakuuzani kuti, ‘Musabwererenso kudzera njira iyi.’

  • 2 Samueli 8:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Davide anagwira amuna 1,700 okwera pamahatchi ndi amuna 20,000 oyenda pansi+ a Hadadezeri. Kenako Davide anapundula*+ mahatchi onse a magaleta+ kusiyapo mahatchi a magaleta okwana 100.

  • 1 Mafumu 10:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Aliyense anali kubweretsa mphatso+ chaka chilichonse+ monga zinthu zasiliva,+ zinthu zagolide, zovala, zida zankhondo,+ mafuta a basamu, mahatchi, ndi nyulu.+

  • 2 Mbiri 1:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Nthawi ndi nthawi anali kugula galeta lochokera ku Iguputo pamtengo wa ndalama zasiliva 600. Hatchi anali kuigula pamtengo wa ndalama zasiliva 150. Umu ndi mmene mafumu onse a Ahiti ndi mafumu a ku Siriya+ anali kuchitira. Mafumuwa anali kugwiritsa ntchito amalondawo pogula zinthuzo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena