Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Chonde, tsegulani maso anu ndi kutchera khutu+ kuti mumve pemphero la ine mtumiki wanu+ limene ndikupemphera pamaso panu lero. Usana ndi usiku+ ndikupempherera atumiki anu, ana a Isiraeli. Pochita zimenezi ndikuvomereza+ machimo+ a ana a Isiraeli amene tinakuchimwirani. Tonse tinachimwa, ine pamodzi ndi nyumba ya bambo anga.+

  • Salimo 106:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Tachimwa mofanana ndi makolo athu.+

      Tachita zinthu zosayenera, tachita zinthu zoipa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena