Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 24:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Tsopano opani Yehova+ ndi kum’tumikira mosalakwitsa ndiponso mokhulupirika.*+ Chotsani milungu imene makolo anu ankatumikira kutsidya lina la Mtsinje ndi ku Iguputo,+ ndipo tumikirani Yehova.

  • Ezara 4:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 nthawi yomweyo anapita kwa Zerubabele+ ndi kwa atsogoleri+ a nyumba za makolo n’kukawauza kuti: “Bwanji timangire nanu limodzi,+ popeza ifeyo mofanana ndi inuyo, timapembedza Mulungu wanu+ ndipo timapereka nsembe kwa iye, kuyambira m’masiku a Esari-hadoni+ mfumu ya Asuri, yemwe anatibweretsa kuno.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena