26 Kodi sunamve?+ Kuyambira nthawi zakale izi n’zimene ndidzachite.+
Ndinakonza zimenezi kuyambira masiku amakedzana.+ Tsopano ndizichita.+
Iweyo udzagwira ntchito yosandutsa mizinda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri, kukhala yopanda anthu ngati milu ya mabwinja.+