25 Kodi sunamve?+ Kuyambira nthawi zakale, izi n’zimene ndidzachite.+
Ndinakonza zimenezi kuyambira masiku amakedzana.+
Tsopano ndizichita.+
Iweyo udzagwira ntchito yosandutsa mizinda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri, kukhala yopanda anthu ngati milu ya mabwinja.+