Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 19:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Kodi sunamve?+ Kuyambira nthawi zakale, izi n’zimene ndidzachite.+

      Ndinakonza zimenezi kuyambira masiku amakedzana.+

      Tsopano ndizichita.+

      Iweyo udzagwira ntchito yosandutsa mizinda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri, kukhala yopanda anthu ngati milu ya mabwinja.+

  • Salimo 33:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Zolinga za Yehova zidzakhalapo mpaka kalekale.+

      Maganizo a mumtima mwake adzakhalapo ku mibadwomibadwo.+

  • Yesaya 46:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ine ndi amene ndidzaitane mbalame yodya nyama kuchokera kotulukira dzuwa.+ Ndidzaitana munthu kuti adzachite zolingalira zanga kuchokera kutali.+ Ineyo ndalankhula ndipo ndidzazichita.+ Ndakonza zimenezi ndipo ndidzazichitadi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena